Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shams ayat 2 - الشَّمس - Page - Juz 30
﴿وَٱلۡقَمَرِ إِذَا تَلَىٰهَا ﴾
[الشَّمس: 2]
﴿والقمر إذا تلاها﴾ [الشَّمس: 2]
Khaled Ibrahim Betala “Ndi mwezi pamene ukulitsatira (dzuwalo ndikulowa mmalo mwake powalitsa dziko dzuwalo litalowa) |