×

Surah An-Naziat in Chichewa

Quran Chichewa ⮕ Surah Naziat

Translation of the Meanings of Surah Naziat in Chichewa - نيانجا

The Quran in Chichewa - Surah Naziat translated into Chichewa, Surah An-Naziat in Chichewa. We provide accurate translation of Surah Naziat in Chichewa - نيانجا, Verses 46 - Surah Number 79 - Page 583.

بسم الله الرحمن الرحيم

وَالنَّازِعَاتِ غَرْقًا (1)
Pali iwo amene amalanda mwankhanza
وَالنَّاشِطَاتِ نَشْطًا (2)
Ndi pali iwo amene amachotsa mwaufulu
وَالسَّابِحَاتِ سَبْحًا (3)
Ndi pali iwo amene amauluka
فَالسَّابِقَاتِ سَبْقًا (4)
Ndi pali iwo amene amathamanga ngati ali pa liwiro loopsya
فَالْمُدَبِّرَاتِ أَمْرًا (5)
Ndi pali angelo amene amakwaniritsa kuchita malamulo a Ambuye wawo
يَوْمَ تَرْجُفُ الرَّاجِفَةُ (6)
Patsiku limene dziko ndi mapiri zidzagwedezeka kwambiri
تَتْبَعُهَا الرَّادِفَةُ (7)
Ndi kulira kwa lipenga kawiri
قُلُوبٌ يَوْمَئِذٍ وَاجِفَةٌ (8)
Mitima, patsiku limeneli, idzafumuka ndi kuda nkhawa
أَبْصَارُهَا خَاشِعَةٌ (9)
Maso awo atagwetsa pansi
يَقُولُونَ أَإِنَّا لَمَرْدُودُونَ فِي الْحَافِرَةِ (10)
Iwo amanena kuti: “Kodi ife tidzabwerera monga momwe tinali poyamba?”
أَإِذَا كُنَّا عِظَامًا نَّخِرَةً (11)
“Angakhale mafupa athu ataola?”
قَالُوا تِلْكَ إِذًا كَرَّةٌ خَاسِرَةٌ (12)
Iwo amati: “Kubwerera kotero ndi kopanda phindu.”
فَإِنَّمَا هِيَ زَجْرَةٌ وَاحِدَةٌ (13)
Koma udzakhala mfuwu umodzi okha
فَإِذَا هُم بِالسَّاهِرَةِ (14)
Pamene, taona, iwo adzadzipeza okha ali pamwamba pa nthaka ali ndi moyo
هَلْ أَتَاكَ حَدِيثُ مُوسَىٰ (15)
Kodiinumudaimvankhaniya Mose
إِذْ نَادَاهُ رَبُّهُ بِالْوَادِ الْمُقَدَّسِ طُوًى (16)
PameneAmbuye wake adamuitana mu dambo lodalitsika la Tuwa
اذْهَبْ إِلَىٰ فِرْعَوْنَ إِنَّهُ طَغَىٰ (17)
“Pita kwa Farao; Ndithudi iye waphwanya malamulo mopyola muyezo.”
فَقُلْ هَل لَّكَ إِلَىٰ أَن تَزَكَّىٰ (18)
“Ndipo ukamuuze kuti: Kodi ungadziyeretse wekha?”
وَأَهْدِيَكَ إِلَىٰ رَبِّكَ فَتَخْشَىٰ (19)
“Ndi kuti ine ndikulondolere kwa Ambuye wako kuti uzimuopa Iye?”
فَأَرَاهُ الْآيَةَ الْكُبْرَىٰ (20)
Kotero iye adamuonetsa chizindikiro cha chikulu
فَكَذَّبَ وَعَصَىٰ (21)
Koma iye adachikana ndipo sanamvere
ثُمَّ أَدْبَرَ يَسْعَىٰ (22)
Iye adapitirizabe kuchita zoipa
فَحَشَرَ فَنَادَىٰ (23)
Ndipo iye adaitana anthu ake onse ndipo anafuula mokweza
فَقَالَ أَنَا رَبُّكُمُ الْأَعْلَىٰ (24)
Nati: “Ine ndine Ambuye wanu wapamwamba mwamba.” Al-Naziat
فَأَخَذَهُ اللَّهُ نَكَالَ الْآخِرَةِ وَالْأُولَىٰ (25)
Motero Mulungu adamugwetsera iye chilango chifukwa cha mau ake omaliza ndi oyamba
إِنَّ فِي ذَٰلِكَ لَعِبْرَةً لِّمَن يَخْشَىٰ (26)
Ndithudi mu izi muli phunziro lomveka kwa anthu oopa Mulungu
أَأَنتُمْ أَشَدُّ خَلْقًا أَمِ السَّمَاءُ ۚ بَنَاهَا (27)
Kodi inu ndinu ovuta kulenga kapena thambo la mlengalenga limene Mulungu adalilenga
رَفَعَ سَمْكَهَا فَسَوَّاهَا (28)
Iye analikweza m’mwamba ndi kulikonza bwino
وَأَغْطَشَ لَيْلَهَا وَأَخْرَجَ ضُحَاهَا (29)
Usiku wake amaukuta ndi m’dima ndipo masana ake amatulutsa kuwala
وَالْأَرْضَ بَعْدَ ذَٰلِكَ دَحَاهَا (30)
Ndipo pambuyo pake adalikulitsa dziko
أَخْرَجَ مِنْهَا مَاءَهَا وَمَرْعَاهَا (31)
Ndipo anatulutsa madzi ndi msipu
وَالْجِبَالَ أَرْسَاهَا (32)
Ndipo adazika mapiri molimbika
مَتَاعًا لَّكُمْ وَلِأَنْعَامِكُمْ (33)
Chakudya cha phindu kwa inu ndi kwa zoweta zanu
فَإِذَا جَاءَتِ الطَّامَّةُ الْكُبْرَىٰ (34)
Koma pamene mavuto akulu akudza
يَوْمَ يَتَذَكَّرُ الْإِنسَانُ مَا سَعَىٰ (35)
Tsiku limene munthu adzayamba kuganiza ntchito zake zonse
وَبُرِّزَتِ الْجَحِيمُ لِمَن يَرَىٰ (36)
Ndipo Gahena idzabweretsedwa pafupi kuti aliyense aione
فَأَمَّا مَن طَغَىٰ (37)
Ndipo kwa iye ophwanya malamulo
وَآثَرَ الْحَيَاةَ الدُّنْيَا (38)
Ndipo anasankha moyo wapadziko lino
فَإِنَّ الْجَحِيمَ هِيَ الْمَأْوَىٰ (39)
Ndithudi malo ake okhala ndi ku Gahena
وَأَمَّا مَنْ خَافَ مَقَامَ رَبِّهِ وَنَهَى النَّفْسَ عَنِ الْهَوَىٰ (40)
Koma kwa iwo amene amaopa kukaima pamaso pa Ambuye wake ndi machimo ndipo anali kudziletsa kuchita chifuniro chopanda pake
فَإِنَّ الْجَنَّةَ هِيَ الْمَأْوَىٰ (41)
Ndithudi adzakhala ku Paradiso
يَسْأَلُونَكَ عَنِ السَّاعَةِ أَيَّانَ مُرْسَاهَا (42)
Amakufunsa za nthawi imene chigumula chidzabwere
فِيمَ أَنتَ مِن ذِكْرَاهَا (43)
Iwe siudziwa zoti unene china chili chonse
إِلَىٰ رَبِّكَ مُنتَهَاهَا (44)
Ndi Ambuye wako yekha amene amadziwa tsiku
إِنَّمَا أَنتَ مُنذِرُ مَن يَخْشَاهَا (45)
Iwe ndiwe mchenjezi chabe kwa iwo amene ali kuliopa tsikuli
كَأَنَّهُمْ يَوْمَ يَرَوْنَهَا لَمْ يَلْبَثُوا إِلَّا عَشِيَّةً أَوْ ضُحَاهَا (46)
Patsiku limene iwo adzachiona chigumula, kudzakhala ngati kuti iwo sanakhale padziko lapansi nthawi yaitali koma usiku umodzi kapena usana wokha
❮ Previous Next ❯

Surahs from Quran :

1- Fatiha2- Baqarah
3- Al Imran4- Nisa
5- Maidah6- Anam
7- Araf8- Anfal
9- Tawbah10- Yunus
11- Hud12- Yusuf
13- Raad14- Ibrahim
15- Hijr16- Nahl
17- Al Isra18- Kahf
19- Maryam20- TaHa
21- Anbiya22- Hajj
23- Muminun24- An Nur
25- Furqan26- Shuara
27- Naml28- Qasas
29- Ankabut30- Rum
31- Luqman32- Sajdah
33- Ahzab34- Saba
35- Fatir36- Yasin
37- Assaaffat38- Sad
39- Zumar40- Ghafir
41- Fussilat42- shura
43- Zukhruf44- Ad Dukhaan
45- Jathiyah46- Ahqaf
47- Muhammad48- Al Fath
49- Hujurat50- Qaf
51- zariyat52- Tur
53- Najm54- Al Qamar
55- Rahman56- Waqiah
57- Hadid58- Mujadilah
59- Al Hashr60- Mumtahina
61- Saff62- Jumuah
63- Munafiqun64- Taghabun
65- Talaq66- Tahrim
67- Mulk68- Qalam
69- Al-Haqqah70- Maarij
71- Nuh72- Jinn
73- Muzammil74- Muddathir
75- Qiyamah76- Insan
77- Mursalat78- An Naba
79- Naziat80- Abasa
81- Takwir82- Infitar
83- Mutaffifin84- Inshiqaq
85- Buruj86- Tariq
87- Al Ala88- Ghashiya
89- Fajr90- Al Balad
91- Shams92- Lail
93- Duha94- Sharh
95- Tin96- Al Alaq
97- Qadr98- Bayyinah
99- Zalzalah100- Adiyat
101- Qariah102- Takathur
103- Al Asr104- Humazah
105- Al Fil106- Quraysh
107- Maun108- Kawthar
109- Kafirun110- Nasr
111- Masad112- Ikhlas
113- Falaq114- An Nas