×

Surah Al-Burooj in Chichewa

Quran Chichewa ⮕ Surah Buruj

Translation of the Meanings of Surah Buruj in Chichewa - نيانجا

The Quran in Chichewa - Surah Buruj translated into Chichewa, Surah Al-Burooj in Chichewa. We provide accurate translation of Surah Buruj in Chichewa - نيانجا, Verses 22 - Surah Number 85 - Page 590.

بسم الله الرحمن الرحيم

وَالسَّمَاءِ ذَاتِ الْبُرُوجِ (1)
Pali kumwamba kumene kuli nyenyezi zikulu zikulu
وَالْيَوْمِ الْمَوْعُودِ (2)
Pali tsiku lolonjezedwa
وَشَاهِدٍ وَمَشْهُودٍ (3)
Pali tsiku la umboni ndi tsiku loperekedwa umboni
قُتِلَ أَصْحَابُ الْأُخْدُودِ (4)
wotembereredwa anali anthu amene anakumba ngalande
النَّارِ ذَاتِ الْوَقُودِ (5)
Imene munali moto woyaka
إِذْ هُمْ عَلَيْهَا قُعُودٌ (6)
Pamene akhala moizungulira
وَهُمْ عَلَىٰ مَا يَفْعَلُونَ بِالْمُؤْمِنِينَ شُهُودٌ (7)
Ndipo iwo adachitira umboni pa zomwe amachitira anthu okhulupirira
وَمَا نَقَمُوا مِنْهُمْ إِلَّا أَن يُؤْمِنُوا بِاللَّهِ الْعَزِيزِ الْحَمِيدِ (8)
Iwo analibe mlandu wina uliwonse ndi anthuwa kupatula kuti anali kukhulupirira mwa Mulungu mmodzi yekha, Mwini mphamvu zonse, Mwini kuyamikidwa
الَّذِي لَهُ مُلْكُ السَّمَاوَاتِ وَالْأَرْضِ ۚ وَاللَّهُ عَلَىٰ كُلِّ شَيْءٍ شَهِيدٌ (9)
Mwini Ufumu wakumwamba ndi dziko lapansi! Ndipo Mulungu ndi mboni pa chilichonse
إِنَّ الَّذِينَ فَتَنُوا الْمُؤْمِنِينَ وَالْمُؤْمِنَاتِ ثُمَّ لَمْ يَتُوبُوا فَلَهُمْ عَذَابُ جَهَنَّمَ وَلَهُمْ عَذَابُ الْحَرِيقِ (10)
Ndithudi onse amene adazunza amuna okhulupirira, ndi akazi okhulupilira ndipo salapa machimo awo, adzalandira chilango chowawa cha moto woyaka wa ku Gahena
إِنَّ الَّذِينَ آمَنُوا وَعَمِلُوا الصَّالِحَاتِ لَهُمْ جَنَّاتٌ تَجْرِي مِن تَحْتِهَا الْأَنْهَارُ ۚ ذَٰلِكَ الْفَوْزُ الْكَبِيرُ (11)
Ndithu onse amene akhulupirira ndi kuchita ntchito zabwino adzakhala m’minda imene ili ndi mitsinje ya madzi oyenda. Kumeneko ndiko kupambana kwakukulu
إِنَّ بَطْشَ رَبِّكَ لَشَدِيدٌ (12)
Ndithudi chilango cha Ambuye wako ndi chowawa
إِنَّهُ هُوَ يُبْدِئُ وَيُعِيدُ (13)
Ndithudi Iye ndiye amene amayambitsa chilengedwe ndipo adzachibwereza patsiku louka kwa akufa
وَهُوَ الْغَفُورُ الْوَدُودُ (14)
Ndipo Iye ndi wokhululuka ndi wachikondi chodzadza
ذُو الْعَرْشِ الْمَجِيدُ (15)
Mwini wake wa Mpando wachifumu, Wolemekezeka
فَعَّالٌ لِّمَا يُرِيدُ (16)
Iye amachita chimene afuna
هَلْ أَتَاكَ حَدِيثُ الْجُنُودِ (17)
Kodi iwe siudamve za asirikali
فِرْعَوْنَ وَثَمُودَ (18)
A Farao ndi a Thamoud
بَلِ الَّذِينَ كَفَرُوا فِي تَكْذِيبٍ (19)
Iyayi! Koma anthu osakhulupirira amazikana
وَاللَّهُ مِن وَرَائِهِم مُّحِيطٌ (20)
Ndipo Mulungu amawazungulira onse
بَلْ هُوَ قُرْآنٌ مَّجِيدٌ (21)
Iyayi! Ili ndi Buku loyera la Korani
فِي لَوْحٍ مَّحْفُوظٍ (22)
Lolembedwa m’Buku lotetezedwa
❮ Previous Next ❯

Surahs from Quran :

1- Fatiha2- Baqarah
3- Al Imran4- Nisa
5- Maidah6- Anam
7- Araf8- Anfal
9- Tawbah10- Yunus
11- Hud12- Yusuf
13- Raad14- Ibrahim
15- Hijr16- Nahl
17- Al Isra18- Kahf
19- Maryam20- TaHa
21- Anbiya22- Hajj
23- Muminun24- An Nur
25- Furqan26- Shuara
27- Naml28- Qasas
29- Ankabut30- Rum
31- Luqman32- Sajdah
33- Ahzab34- Saba
35- Fatir36- Yasin
37- Assaaffat38- Sad
39- Zumar40- Ghafir
41- Fussilat42- shura
43- Zukhruf44- Ad Dukhaan
45- Jathiyah46- Ahqaf
47- Muhammad48- Al Fath
49- Hujurat50- Qaf
51- zariyat52- Tur
53- Najm54- Al Qamar
55- Rahman56- Waqiah
57- Hadid58- Mujadilah
59- Al Hashr60- Mumtahina
61- Saff62- Jumuah
63- Munafiqun64- Taghabun
65- Talaq66- Tahrim
67- Mulk68- Qalam
69- Al-Haqqah70- Maarij
71- Nuh72- Jinn
73- Muzammil74- Muddathir
75- Qiyamah76- Insan
77- Mursalat78- An Naba
79- Naziat80- Abasa
81- Takwir82- Infitar
83- Mutaffifin84- Inshiqaq
85- Buruj86- Tariq
87- Al Ala88- Ghashiya
89- Fajr90- Al Balad
91- Shams92- Lail
93- Duha94- Sharh
95- Tin96- Al Alaq
97- Qadr98- Bayyinah
99- Zalzalah100- Adiyat
101- Qariah102- Takathur
103- Al Asr104- Humazah
105- Al Fil106- Quraysh
107- Maun108- Kawthar
109- Kafirun110- Nasr
111- Masad112- Ikhlas
113- Falaq114- An Nas