×

Ndipo, ndithudi, pakati pawo pali iwo amene amatembenuza tanthauzo la Buku ndi 3:78 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:78) ayat 78 in Chichewa

3:78 Surah al-‘Imran ayat 78 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 78 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿وَإِنَّ مِنۡهُمۡ لَفَرِيقٗا يَلۡوُۥنَ أَلۡسِنَتَهُم بِٱلۡكِتَٰبِ لِتَحۡسَبُوهُ مِنَ ٱلۡكِتَٰبِ وَمَا هُوَ مِنَ ٱلۡكِتَٰبِ وَيَقُولُونَ هُوَ مِنۡ عِندِ ٱللَّهِ وَمَا هُوَ مِنۡ عِندِ ٱللَّهِۖ وَيَقُولُونَ عَلَى ٱللَّهِ ٱلۡكَذِبَ وَهُمۡ يَعۡلَمُونَ ﴾
[آل عِمران: 78]

Ndipo, ndithudi, pakati pawo pali iwo amene amatembenuza tanthauzo la Buku ndi malirime awo pamene akuwerenga ndi cholinga chakuti iwe uziganiza kuti zonse zimene ali kunena ndi zochokera m’Buku pamene sichoncho ayi, ndipo iwo amati: “Mawu awa ndi ochokera kwa Mulungu” pamene sadachokere kwa Mulungu ndipo iwo amanena zabodza zokhudza Mulungu pamene iwo akudziwa kuti limenelo ndi bodza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإن منهم لفريقا يلوون ألسنتهم بالكتاب لتحسبوه من الكتاب وما هو من, باللغة نيانجا

﴿وإن منهم لفريقا يلوون ألسنتهم بالكتاب لتحسبوه من الكتاب وما هو من﴾ [آل عِمران: 78]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu mwa iwo muli gulu lomwe likukhotetsa malirime awo (powerenga) buku kuti muwaganizire (mawu awowo) kuti ndi a m’buku la Allah); pomwe si a m’buku (la Allah). Ndipo akunena: “Izi zachokera kwa Allah.” Pomwe zimenezo sizinachokere kwa Allah; ndipo akumnamizira Allah uku akudziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek