×

Ndipo mu ilo, Ife tidalamula kuti moyo ku moyo, diso ku diso, 5:45 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:45) ayat 45 in Chichewa

5:45 Surah Al-Ma’idah ayat 45 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 45 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿وَكَتَبۡنَا عَلَيۡهِمۡ فِيهَآ أَنَّ ٱلنَّفۡسَ بِٱلنَّفۡسِ وَٱلۡعَيۡنَ بِٱلۡعَيۡنِ وَٱلۡأَنفَ بِٱلۡأَنفِ وَٱلۡأُذُنَ بِٱلۡأُذُنِ وَٱلسِّنَّ بِٱلسِّنِّ وَٱلۡجُرُوحَ قِصَاصٞۚ فَمَن تَصَدَّقَ بِهِۦ فَهُوَ كَفَّارَةٞ لَّهُۥۚ وَمَن لَّمۡ يَحۡكُم بِمَآ أَنزَلَ ٱللَّهُ فَأُوْلَٰٓئِكَ هُمُ ٱلظَّٰلِمُونَ ﴾
[المَائدة: 45]

Ndipo mu ilo, Ife tidalamula kuti moyo ku moyo, diso ku diso, mphuno ku mphuno, khutu ku khutu, dzino ku dzino ndi ululu ku ululu. Koma ngati munthu akhululuka chifukwa chowonetsa chisoni, chimenechi chidzakhala chikhululukiro. Ndipo aliyense amene saweruza ndi zomwe adavumbulutsa Mulungu, woteroyo ndi opanda chilungamo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وكتبنا عليهم فيها أن النفس بالنفس والعين بالعين والأنف بالأنف والأذن بالأذن, باللغة نيانجا

﴿وكتبنا عليهم فيها أن النفس بالنفس والعين بالعين والأنف بالأنف والأذن بالأذن﴾ [المَائدة: 45]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek