×

Ndipo tikadafuna Ife tikadamukweza iye, koma iye adaumirira moyo wa pa dziko 7:176 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:176) ayat 176 in Chichewa

7:176 Surah Al-A‘raf ayat 176 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 176 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿وَلَوۡ شِئۡنَا لَرَفَعۡنَٰهُ بِهَا وَلَٰكِنَّهُۥٓ أَخۡلَدَ إِلَى ٱلۡأَرۡضِ وَٱتَّبَعَ هَوَىٰهُۚ فَمَثَلُهُۥ كَمَثَلِ ٱلۡكَلۡبِ إِن تَحۡمِلۡ عَلَيۡهِ يَلۡهَثۡ أَوۡ تَتۡرُكۡهُ يَلۡهَثۚ ذَّٰلِكَ مَثَلُ ٱلۡقَوۡمِ ٱلَّذِينَ كَذَّبُواْ بِـَٔايَٰتِنَاۚ فَٱقۡصُصِ ٱلۡقَصَصَ لَعَلَّهُمۡ يَتَفَكَّرُونَ ﴾
[الأعرَاف: 176]

Ndipo tikadafuna Ife tikadamukweza iye, koma iye adaumirira moyo wa pa dziko lino lapansi ndi kutsatira zilakolako zake. Motero iye akhoza kufanizidwa ndi galu, amene ngati umupilikitsa, amatulutsa lilime lake, kaya umusiya yekha iye amalitulutsabe. Limenelo ndi fanizo la anthu amene amakana zizindikiro zathu. Motero auze nkhanizi kuti mwina iwo akhoza kuganiza bwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو شئنا لرفعناه بها ولكنه أخلد إلى الأرض واتبع هواه فمثله كمثل, باللغة نيانجا

﴿ولو شئنا لرفعناه بها ولكنه أخلد إلى الأرض واتبع هواه فمثله كمثل﴾ [الأعرَاف: 176]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tikadafuna tikadamtukula nazo (ulemelero wake). Koma iye adapendekera ku za mdziko natsatira zilakolako zake. Fanizo lake lili ngati galu. Ngati utamkalipira amathawa uku akutulutsa lirime lake kunja. Ngakhale utamsiya amatulutsabe kunja lirime lake. Umo ndi momwe liliri fanizo la anthu otsutsa zizindikiro Zathu. Choncho asimbire nkhani izi kuti angalingalire
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek