×

Choperekachaulerechiperekedwe kwa osauka amene atangwanika ndi ntchito ya Mulungu ndipo sangathe kuyenda 2:273 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Baqarah ⮕ (2:273) ayat 273 in Chichewa

2:273 Surah Al-Baqarah ayat 273 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Baqarah ayat 273 - البَقَرَة - Page - Juz 3

﴿لِلۡفُقَرَآءِ ٱلَّذِينَ أُحۡصِرُواْ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ لَا يَسۡتَطِيعُونَ ضَرۡبٗا فِي ٱلۡأَرۡضِ يَحۡسَبُهُمُ ٱلۡجَاهِلُ أَغۡنِيَآءَ مِنَ ٱلتَّعَفُّفِ تَعۡرِفُهُم بِسِيمَٰهُمۡ لَا يَسۡـَٔلُونَ ٱلنَّاسَ إِلۡحَافٗاۗ وَمَا تُنفِقُواْ مِنۡ خَيۡرٖ فَإِنَّ ٱللَّهَ بِهِۦ عَلِيمٌ ﴾
[البَقَرَة: 273]

Choperekachaulerechiperekedwe kwa osauka amene atangwanika ndi ntchito ya Mulungu ndipo sangathe kuyenda padziko. Munthu amene sawadziwa amaganiza kuti, chifukwa chodzichepetsa kwawo, iwo sasowa chilichonse. Iwe udzawadziwa chifukwa cha maonekedwe awo. Iwo sapempha ayi. Ndipo chilichonse chabwino chimene upereka, ndithudi Mulungu amachidziwa bwino kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: للفقراء الذين أحصروا في سبيل الله لا يستطيعون ضربا في الأرض يحسبهم, باللغة نيانجا

﴿للفقراء الذين أحصروا في سبيل الله لا يستطيعون ضربا في الأرض يحسبهم﴾ [البَقَرَة: 273]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek