×

oh inu anthu okhulupirira! Lolani akapolo anu aamuna ndi aakazi ndi ana 24:58 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:58) ayat 58 in Chichewa

24:58 Surah An-Nur ayat 58 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 58 - النور - Page - Juz 18

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لِيَسۡتَـٔۡذِنكُمُ ٱلَّذِينَ مَلَكَتۡ أَيۡمَٰنُكُمۡ وَٱلَّذِينَ لَمۡ يَبۡلُغُواْ ٱلۡحُلُمَ مِنكُمۡ ثَلَٰثَ مَرَّٰتٖۚ مِّن قَبۡلِ صَلَوٰةِ ٱلۡفَجۡرِ وَحِينَ تَضَعُونَ ثِيَابَكُم مِّنَ ٱلظَّهِيرَةِ وَمِنۢ بَعۡدِ صَلَوٰةِ ٱلۡعِشَآءِۚ ثَلَٰثُ عَوۡرَٰتٖ لَّكُمۡۚ لَيۡسَ عَلَيۡكُمۡ وَلَا عَلَيۡهِمۡ جُنَاحُۢ بَعۡدَهُنَّۚ طَوَّٰفُونَ عَلَيۡكُم بَعۡضُكُمۡ عَلَىٰ بَعۡضٖۚ كَذَٰلِكَ يُبَيِّنُ ٱللَّهُ لَكُمُ ٱلۡأٓيَٰتِۗ وَٱللَّهُ عَلِيمٌ حَكِيمٞ ﴾
[النور: 58]

oh inu anthu okhulupirira! Lolani akapolo anu aamuna ndi aakazi ndi ana amene sanathe msinkhu kuti apemphe poyamba pa nthawi zitatu, musadapemphere pemphero la m’mawa kapena pamene mwavula zovala zanu masana chifukwa cha kutentha kapena mutatha kupemphera mapemphero a usiku. Izi ndi nthawi zitatu zokhala panokha. Palibe chifukwa kwa inu kapena kwa iwo kuchezerana, wina ndi mnzake mu nthawi zina kupatula nthawi zimene zatchulidwazi. Kotero Mulungu amaulula poyera chivumbulutso chake kwa inu. Ndipo Mulungu ndi Wodziwa ndi Waluntha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا ليستأذنكم الذين ملكت أيمانكم والذين لم يبلغوا الحلم منكم, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا ليستأذنكم الذين ملكت أيمانكم والذين لم يبلغوا الحلم منكم﴾ [النور: 58]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Akuodireni amene manja anu akumanja apeza ndi amene mwa inu sanathe nsinkhu, awodire nthawi zitatu: Isanapempheredwe Swala ya m’mawa, ndi pamene mukuvula nsalu zanu nthawi yamasana (kuti mupumule), ndi pambuyo pa Swala ya Isha (usiku). Izi ndi nthawi zitatu zomwe inu mumakhala wamba. Palibe uchimo pa inu ngakhale pa iwo pambuyo pa nthawi zimenezo (kulowa popanda kuodira); mumazungulirana pakati panu, umo ndi momwe akukufotokozerani Allah Ayah (ndime) Zake. Ndipo Allah Ngodziwa; Ngwanzeru zakuya
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek