Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shu‘ara’ ayat 70 - الشعراء - Page - Juz 19
﴿إِذۡ قَالَ لِأَبِيهِ وَقَوۡمِهِۦ مَا تَعۡبُدُونَ ﴾
[الشعراء: 70]
﴿إذ قال لأبيه وقومه ما تعبدون﴾ [الشعراء: 70]
Khaled Ibrahim Betala “Pamene adafunsa bambo wake ndi anthu ake (kuti); “Kodi mukupembedza chiyani?” |