×

Zokoma kwa amuna ndi chikondi chimene ali nacho pa zinthu zimene apeza, 3:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:14) ayat 14 in Chichewa

3:14 Surah al-‘Imran ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 14 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿زُيِّنَ لِلنَّاسِ حُبُّ ٱلشَّهَوَٰتِ مِنَ ٱلنِّسَآءِ وَٱلۡبَنِينَ وَٱلۡقَنَٰطِيرِ ٱلۡمُقَنطَرَةِ مِنَ ٱلذَّهَبِ وَٱلۡفِضَّةِ وَٱلۡخَيۡلِ ٱلۡمُسَوَّمَةِ وَٱلۡأَنۡعَٰمِ وَٱلۡحَرۡثِۗ ذَٰلِكَ مَتَٰعُ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَاۖ وَٱللَّهُ عِندَهُۥ حُسۡنُ ٱلۡمَـَٔابِ ﴾
[آل عِمران: 14]

Zokoma kwa amuna ndi chikondi chimene ali nacho pa zinthu zimene apeza, akazi, ana, chuma cha golide ndi siliva chimene chasonkhanitsidwa, mahatchi okongola, ziweto ndipo minda yolimidwa bwino. Ichi ndi chisangalalo cha m’moyo uno koma Mulungu ali ndi zinthu zabwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: زين للناس حب الشهوات من النساء والبنين والقناطير المقنطرة من الذهب والفضة, باللغة نيانجا

﴿زين للناس حب الشهوات من النساء والبنين والقناطير المقنطرة من الذهب والفضة﴾ [آل عِمران: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Kwakometsedwa kwa anthu kukonda zilakolako (za moyo wawo) monga akazi, ana, milumilu ya chuma cha golide ndi siliva, ndi mahachi oyang’aniridwa bwino, ziweto ndi mbewu. Izo ndi zosangalatsa za moyo wa dziko lapansi (zomwe sizili kanthu). Koma kwa Allah ndiko kuli mabwelero abwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek