×

Kodi iwo sadayende pa dziko ndi kuona zimene zidawaonekera anthu amene adalipo 30:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:9) ayat 9 in Chichewa

30:9 Surah Ar-Rum ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 9 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿أَوَلَمۡ يَسِيرُواْ فِي ٱلۡأَرۡضِ فَيَنظُرُواْ كَيۡفَ كَانَ عَٰقِبَةُ ٱلَّذِينَ مِن قَبۡلِهِمۡۚ كَانُوٓاْ أَشَدَّ مِنۡهُمۡ قُوَّةٗ وَأَثَارُواْ ٱلۡأَرۡضَ وَعَمَرُوهَآ أَكۡثَرَ مِمَّا عَمَرُوهَا وَجَآءَتۡهُمۡ رُسُلُهُم بِٱلۡبَيِّنَٰتِۖ فَمَا كَانَ ٱللَّهُ لِيَظۡلِمَهُمۡ وَلَٰكِن كَانُوٓاْ أَنفُسَهُمۡ يَظۡلِمُونَ ﴾
[الرُّوم: 9]

Kodi iwo sadayende pa dziko ndi kuona zimene zidawaonekera anthu amene adalipo kale? Iwo adali ndi mphamvu zambiri kuposa awa, ndipo adakumba nthaka ndiponso adamanga pa nthakayo nyumba zambiri kuposa zimene awa amanga. Ndipo kudadza kwa iwo Atumwi awo ndi chiphunzitso chomveka ndipo sikudali koyenera kuti Mulungu awachitire zinthu zosalungama koma kuti iwo adalakwira mizimu yawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أو لم يسيروا في الأرض فينظروا كيف كان عاقبة الذين من قبلهم, باللغة نيانجا

﴿أو لم يسيروا في الأرض فينظروا كيف كان عاقبة الذين من قبلهم﴾ [الرُّوم: 9]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek