×

Anthuamakufunsanizaola. Nenakuti,“Mulunguyekha ndiye amene amadziwa za ilo. Kodi chidzakudziwitsani ndi chiyani za 33:63 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:63) ayat 63 in Chichewa

33:63 Surah Al-Ahzab ayat 63 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 63 - الأحزَاب - Page - Juz 22

﴿يَسۡـَٔلُكَ ٱلنَّاسُ عَنِ ٱلسَّاعَةِۖ قُلۡ إِنَّمَا عِلۡمُهَا عِندَ ٱللَّهِۚ وَمَا يُدۡرِيكَ لَعَلَّ ٱلسَّاعَةَ تَكُونُ قَرِيبًا ﴾
[الأحزَاب: 63]

Anthuamakufunsanizaola. Nenakuti,“Mulunguyekha ndiye amene amadziwa za ilo. Kodi chidzakudziwitsani ndi chiyani za olali? Mwinatu lili pafupi!”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يسألك الناس عن الساعة قل إنما علمها عند الله وما يدريك لعل, باللغة نيانجا

﴿يسألك الناس عن الساعة قل إنما علمها عند الله وما يدريك لعل﴾ [الأحزَاب: 63]

Khaled Ibrahim Betala
“Anthu akukufunsa za (kudza kwa) nthawi (ya tsiku la chitsiriziro). Nena: “Kuzindikira kwa nthawiyo kuli ndi Allah (Yekha). Nanga nchiyani chikudziwitse kuti nthawi ya chimaliziro iri pafupi?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek