×

Anthu achinyengo, amuna ndi akazi, onse ndi chimodzimodzi. Iwo amalamulira zinthu zoipa 9:67 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:67) ayat 67 in Chichewa

9:67 Surah At-Taubah ayat 67 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 67 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿ٱلۡمُنَٰفِقُونَ وَٱلۡمُنَٰفِقَٰتُ بَعۡضُهُم مِّنۢ بَعۡضٖۚ يَأۡمُرُونَ بِٱلۡمُنكَرِ وَيَنۡهَوۡنَ عَنِ ٱلۡمَعۡرُوفِ وَيَقۡبِضُونَ أَيۡدِيَهُمۡۚ نَسُواْ ٱللَّهَ فَنَسِيَهُمۡۚ إِنَّ ٱلۡمُنَٰفِقِينَ هُمُ ٱلۡفَٰسِقُونَ ﴾
[التوبَة: 67]

Anthu achinyengo, amuna ndi akazi, onse ndi chimodzimodzi. Iwo amalamulira zinthu zoipa ndi kuletsa zimene zili zabwino ndiponso iwo amaumila. Iwo amuiwala Mulungu, motero nayenso wawaiwala. Ndithudi anthu a chinyengo ndi anthu wochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: المنافقون والمنافقات بعضهم من بعض يأمرون بالمنكر وينهون عن المعروف ويقبضون أيديهم, باللغة نيانجا

﴿المنافقون والمنافقات بعضهم من بعض يأمرون بالمنكر وينهون عن المعروف ويقبضون أيديهم﴾ [التوبَة: 67]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek