×

Motere icho chinayenda pa mafunde okhala ngati mapiri, ndipo Nowa adamuitana mwana 11:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:42) ayat 42 in Chichewa

11:42 Surah Hud ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 42 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَهِيَ تَجۡرِي بِهِمۡ فِي مَوۡجٖ كَٱلۡجِبَالِ وَنَادَىٰ نُوحٌ ٱبۡنَهُۥ وَكَانَ فِي مَعۡزِلٖ يَٰبُنَيَّ ٱرۡكَب مَّعَنَا وَلَا تَكُن مَّعَ ٱلۡكَٰفِرِينَ ﴾
[هُود: 42]

Motere icho chinayenda pa mafunde okhala ngati mapiri, ndipo Nowa adamuitana mwana wake amene adaima pambali. “oh mwana wanga! Kwerachombopamodzindiifendipousakhalepamodzindi anthu osakhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وهي تجري بهم في موج كالجبال ونادى نوح ابنه وكان في معزل, باللغة نيانجا

﴿وهي تجري بهم في موج كالجبال ونادى نوح ابنه وكان في معزل﴾ [هُود: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (chombocho) chidali kuyenda nawo m’mafunde onga mapiri, ndipo Nuh adaitana mwana wake yemwe adali patali (atakana kulowa m’chombo): “Mwana wanga! Kwera pamodzi ndi ife usakhale pamodzi ndi osakhulupirira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek