×

Mmenemo ndi mmene tidamupatsira Yosefe udindo mdziko ndipo adakhala paliponse pamene amafuna. 12:56 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:56) ayat 56 in Chichewa

12:56 Surah Yusuf ayat 56 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 56 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿وَكَذَٰلِكَ مَكَّنَّا لِيُوسُفَ فِي ٱلۡأَرۡضِ يَتَبَوَّأُ مِنۡهَا حَيۡثُ يَشَآءُۚ نُصِيبُ بِرَحۡمَتِنَا مَن نَّشَآءُۖ وَلَا نُضِيعُ أَجۡرَ ٱلۡمُحۡسِنِينَ ﴾
[يُوسُف: 56]

Mmenemo ndi mmene tidamupatsira Yosefe udindo mdziko ndipo adakhala paliponse pamene amafuna. Ife timampatsa chisomo amene tamufuna ndipo sitisokoneza mphotho za anthu ochita zabwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وكذلك مكنا ليوسف في الأرض يتبوأ منها حيث يشاء نصيب برحمتنا من, باللغة نيانجا

﴿وكذلك مكنا ليوسف في الأرض يتبوأ منها حيث يشاء نصيب برحمتنا من﴾ [يُوسُف: 56]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo motero tidampatsa ulemelero Yûsuf m’dziko (la Iguputo); amakhala m’menemo paliponse pamene wafuna. Timam’bweretsera chifundo Chathu amene tamfuna, ndipo sitisokoneza malipiro a ochita zabwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek