×

Pamene iwo adalowa, monga momwe atate awo adawalangizira, sizidawathandize chilichonse kwa Mulungu. 12:68 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:68) ayat 68 in Chichewa

12:68 Surah Yusuf ayat 68 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 68 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿وَلَمَّا دَخَلُواْ مِنۡ حَيۡثُ أَمَرَهُمۡ أَبُوهُم مَّا كَانَ يُغۡنِي عَنۡهُم مِّنَ ٱللَّهِ مِن شَيۡءٍ إِلَّا حَاجَةٗ فِي نَفۡسِ يَعۡقُوبَ قَضَىٰهَاۚ وَإِنَّهُۥ لَذُو عِلۡمٖ لِّمَا عَلَّمۡنَٰهُ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَ ٱلنَّاسِ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[يُوسُف: 68]

Pamene iwo adalowa, monga momwe atate awo adawalangizira, sizidawathandize chilichonse kwa Mulungu. Ichi sichinali china chilichonse koma kungokwaniritsa chifuniro chimene Yakobo adali nacho. Ndithudi iye adali ndi nzeru chifukwa Ife tidamuphunzitsa, koma anthu ambiri sadziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولما دخلوا من حيث أمرهم أبوهم ما كان يغني عنهم من الله, باللغة نيانجا

﴿ولما دخلوا من حيث أمرهم أبوهم ما كان يغني عنهم من الله﴾ [يُوسُف: 68]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pamene adalowa monga momwe bambo wawo adawalamulira, sikudawathandize chilichonse kwa Allah kupatula khumbo lomwe lidali mu mtima mwa Ya’qub (ndilomwe) adalikwaniritsa, (Ya’qub adali kufuna Yûsuf ndi m’bale wake akumane mwamseri; ndipo adakumanadi). Ndithu iye (Ya’qub) adali wanzeru chifukwa chakuti tidamphunzitsa. Koma anthu ambiri sadziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek