×

Iwo ali kukuchititsa iwe kuti uchite choipa m’malo mwa chinthu chabwino. Komatu 13:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Ra‘d ⮕ (13:6) ayat 6 in Chichewa

13:6 Surah Ar-Ra‘d ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Ra‘d ayat 6 - الرَّعد - Page - Juz 13

﴿وَيَسۡتَعۡجِلُونَكَ بِٱلسَّيِّئَةِ قَبۡلَ ٱلۡحَسَنَةِ وَقَدۡ خَلَتۡ مِن قَبۡلِهِمُ ٱلۡمَثُلَٰتُۗ وَإِنَّ رَبَّكَ لَذُو مَغۡفِرَةٖ لِّلنَّاسِ عَلَىٰ ظُلۡمِهِمۡۖ وَإِنَّ رَبَّكَ لَشَدِيدُ ٱلۡعِقَابِ ﴾
[الرَّعد: 6]

Iwo ali kukuchititsa iwe kuti uchite choipa m’malo mwa chinthu chabwino. Komatu ndi anthu ambiri amene adalangidwa iwo asanadze. Ndithudi Ambuye wako amaonetsa chifundo kwa anthu ngakhale kuti iwo ndi ochimwa. Ndithudi Ambuye wako amalangiratu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويستعجلونك بالسيئة قبل الحسنة وقد خلت من قبلهم المثلات وإن ربك لذو, باللغة نيانجا

﴿ويستعجلونك بالسيئة قبل الحسنة وقد خلت من قبلهم المثلات وإن ربك لذو﴾ [الرَّعد: 6]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akukufulumizitsa kuti ubweretse choipa (chomwe ndi chilango chawo) m’malo mwa chabwino; ndithu chikhalirecho zilango zambiri zidapita kale (zomwe akadayenera kuchenjera nazo)! Koma Mbuye wako ndi mwini chikhululuko kwa anthu pa uchimo wawo. Ndipo ndithu Mbuye wako Ngolanga mwaukali
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek