×

Mulungu akupereka fanizo la kapolo amene ali mu ulamuliro wa bwana wake 16:75 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nahl ⮕ (16:75) ayat 75 in Chichewa

16:75 Surah An-Nahl ayat 75 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nahl ayat 75 - النَّحل - Page - Juz 14

﴿۞ ضَرَبَ ٱللَّهُ مَثَلًا عَبۡدٗا مَّمۡلُوكٗا لَّا يَقۡدِرُ عَلَىٰ شَيۡءٖ وَمَن رَّزَقۡنَٰهُ مِنَّا رِزۡقًا حَسَنٗا فَهُوَ يُنفِقُ مِنۡهُ سِرّٗا وَجَهۡرًاۖ هَلۡ يَسۡتَوُۥنَۚ ٱلۡحَمۡدُ لِلَّهِۚ بَلۡ أَكۡثَرُهُمۡ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[النَّحل: 75]

Mulungu akupereka fanizo la kapolo amene ali mu ulamuliro wa bwana wake amene sangathe kuchita chilichonse ndi munthu wina, amene tamupatsa zinthu zabwino ndipo iye amapereka kuchokera ku zimene wapatsidwa mwamseri ndiponso moonekera. Kodi iwo angafanane? Kuyamikidwa konse kukhale kwa Mulungu, koma ambiri a iwo sazindikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ضرب الله مثلا عبدا مملوكا لا يقدر على شيء ومن رزقناه منا, باللغة نيانجا

﴿ضرب الله مثلا عبدا مملوكا لا يقدر على شيء ومن رزقناه منا﴾ [النَّحل: 75]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek