×

Ambuye wa kumwamba ndi dziko lapansi ndi zonse zimene zili mmenemo. Kotero 19:65 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Maryam ⮕ (19:65) ayat 65 in Chichewa

19:65 Surah Maryam ayat 65 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Maryam ayat 65 - مَريَم - Page - Juz 16

﴿رَّبُّ ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضِ وَمَا بَيۡنَهُمَا فَٱعۡبُدۡهُ وَٱصۡطَبِرۡ لِعِبَٰدَتِهِۦۚ هَلۡ تَعۡلَمُ لَهُۥ سَمِيّٗا ﴾
[مَريَم: 65]

Ambuye wa kumwamba ndi dziko lapansi ndi zonse zimene zili mmenemo. Kotero m’pembedze Iye yekha ndipo khala wopirira pamapemphero ake. Kodi ukudziwa wina amene ali ndi dzina ngati la Iye

❮ Previous Next ❯

ترجمة: رب السموات والأرض وما بينهما فاعبده واصطبر لعبادته هل تعلم له سميا, باللغة نيانجا

﴿رب السموات والأرض وما بينهما فاعبده واصطبر لعبادته هل تعلم له سميا﴾ [مَريَم: 65]

Khaled Ibrahim Betala
““Mbuye wa thambo ndi nthaka ndi zapakati pa izo: Choncho mpembedze Iye basi. Ndipo pitiriza ndikupirira popembedza Iye. Kodi ukumudziwa (wina) yemwe ali wofanana Naye (Allah)?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek