×

Kodi wina wa inu angakonde kukhala ndi munda wa tende ndi azitona 2:266 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Baqarah ⮕ (2:266) ayat 266 in Chichewa

2:266 Surah Al-Baqarah ayat 266 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Baqarah ayat 266 - البَقَرَة - Page - Juz 3

﴿أَيَوَدُّ أَحَدُكُمۡ أَن تَكُونَ لَهُۥ جَنَّةٞ مِّن نَّخِيلٖ وَأَعۡنَابٖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ لَهُۥ فِيهَا مِن كُلِّ ٱلثَّمَرَٰتِ وَأَصَابَهُ ٱلۡكِبَرُ وَلَهُۥ ذُرِّيَّةٞ ضُعَفَآءُ فَأَصَابَهَآ إِعۡصَارٞ فِيهِ نَارٞ فَٱحۡتَرَقَتۡۗ كَذَٰلِكَ يُبَيِّنُ ٱللَّهُ لَكُمُ ٱلۡأٓيَٰتِ لَعَلَّكُمۡ تَتَفَكَّرُونَ ﴾
[البَقَرَة: 266]

Kodi wina wa inu angakonde kukhala ndi munda wa tende ndi azitona womwe umathiriridwa ndi mitsinje pansi pake ndipo uli ndi zipatso zosiyanasiyana, pamene ukalamba wampeza, pomwe iye ali ndi ana opanda mphamvu ndipo munda uja uli kukunthidwa ndi mphepo ndipo m’kati mwa mphepoyo muli moto umene utentha mundawo? Kotero Mulungu ali kufotokoza chivumbuluitso chake momveka kwa inu kuti muganize bwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أيود أحدكم أن تكون له جنة من نخيل وأعناب تجري من تحتها, باللغة نيانجا

﴿أيود أحدكم أن تكون له جنة من نخيل وأعناب تجري من تحتها﴾ [البَقَرَة: 266]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek