×

Ku mtundu uliwonse Ife tidalamulira miyambo ya chipembedzo imene iwo ayenera kuitsatira 22:67 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:67) ayat 67 in Chichewa

22:67 Surah Al-hajj ayat 67 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 67 - الحج - Page - Juz 17

﴿لِّكُلِّ أُمَّةٖ جَعَلۡنَا مَنسَكًا هُمۡ نَاسِكُوهُۖ فَلَا يُنَٰزِعُنَّكَ فِي ٱلۡأَمۡرِۚ وَٱدۡعُ إِلَىٰ رَبِّكَۖ إِنَّكَ لَعَلَىٰ هُدٗى مُّسۡتَقِيمٖ ﴾
[الحج: 67]

Ku mtundu uliwonse Ife tidalamulira miyambo ya chipembedzo imene iwo ayenera kuitsatira ndipo iwo asakangane ndi iwe pa nkhani iyi. Koma aitanire kwa Ambuye wako. Ndithudi iwe uli pa njira yoyenera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لكل أمة جعلنا منسكا هم ناسكوه فلا ينازعنك في الأمر وادع إلى, باللغة نيانجا

﴿لكل أمة جعلنا منسكا هم ناسكوه فلا ينازعنك في الأمر وادع إلى﴾ [الحج: 67]

Khaled Ibrahim Betala
“Mpingo uliwonse tidauikira machitidwe amapemphero omwe akuwatsata; choncho asatsutsane nawe pachinthu ichi, ndipo itanira anthu ku chipembedzo cha Mbuye wako. Ndithu iwe uli pachiongoko changwilo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek