×

Sichidzakhala cholakwa kwa amayi okalamba amene alibe maganizo a ukwati ngati angasiye 24:60 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:60) ayat 60 in Chichewa

24:60 Surah An-Nur ayat 60 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 60 - النور - Page - Juz 18

﴿وَٱلۡقَوَٰعِدُ مِنَ ٱلنِّسَآءِ ٱلَّٰتِي لَا يَرۡجُونَ نِكَاحٗا فَلَيۡسَ عَلَيۡهِنَّ جُنَاحٌ أَن يَضَعۡنَ ثِيَابَهُنَّ غَيۡرَ مُتَبَرِّجَٰتِۭ بِزِينَةٖۖ وَأَن يَسۡتَعۡفِفۡنَ خَيۡرٞ لَّهُنَّۗ وَٱللَّهُ سَمِيعٌ عَلِيمٞ ﴾
[النور: 60]

Sichidzakhala cholakwa kwa amayi okalamba amene alibe maganizo a ukwati ngati angasiye zovala zawo zakunja popanda kuonetsa kukongola kwawo. Kungakhale bwino ngati iwo angavale modzilemekeza. Ndipo Mulungu ndi wakumva ndi wodziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والقواعد من النساء اللاتي لا يرجون نكاحا فليس عليهن جناح أن يضعن, باللغة نيانجا

﴿والقواعد من النساء اللاتي لا يرجون نكاحا فليس عليهن جناح أن يضعن﴾ [النور: 60]

Khaled Ibrahim Betala
“Nayonso mikwezembe (nkhalamba zachikhalire zazikazi) yomwe siyembekezera kukwatiwa, palibe uchimo pa iyo kusiya kufunda nsalu zawo (kumutu), popanda kuonetsa zodzikongoletsera zawo. Koma ngati zikudzikakamiza kuleka kuvula mipangoyo, ndibwino kwa iyo. Ndithu Allah Ngwakumva; Ngodziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek