×

“Motero ine ndidathawa inu nonse pa nthawi imene ndidakuopani koma tsopano Ambuye 26:21 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shu‘ara’ ⮕ (26:21) ayat 21 in Chichewa

26:21 Surah Ash-Shu‘ara’ ayat 21 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shu‘ara’ ayat 21 - الشعراء - Page - Juz 19

﴿فَفَرَرۡتُ مِنكُمۡ لَمَّا خِفۡتُكُمۡ فَوَهَبَ لِي رَبِّي حُكۡمٗا وَجَعَلَنِي مِنَ ٱلۡمُرۡسَلِينَ ﴾
[الشعراء: 21]

“Motero ine ndidathawa inu nonse pa nthawi imene ndidakuopani koma tsopano Ambuye wanga wandipatsa luntha ndiponso wandipanga ine kukhala mmodzi mwa Atumwi ake.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ففررت منكم لما خفتكم فوهب لي ربي حكما وجعلني من المرسلين, باللغة نيانجا

﴿ففررت منكم لما خفتكم فوهب لي ربي حكما وجعلني من المرسلين﴾ [الشعراء: 21]

Khaled Ibrahim Betala
““Choncho ndidakuthawani pomwe ndidakuopani; tsono Mbuye wanga wandipatsa nzeru zoweruzira (zinthu), ndi kundisankha kukhala mmodzi wa atumiki.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek