×

Iwo amakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku la chimaliziro, amalamulira zolungama ndi kuletsa 3:114 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:114) ayat 114 in Chichewa

3:114 Surah al-‘Imran ayat 114 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 114 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿يُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِ وَٱلۡيَوۡمِ ٱلۡأٓخِرِ وَيَأۡمُرُونَ بِٱلۡمَعۡرُوفِ وَيَنۡهَوۡنَ عَنِ ٱلۡمُنكَرِ وَيُسَٰرِعُونَ فِي ٱلۡخَيۡرَٰتِۖ وَأُوْلَٰٓئِكَ مِنَ ٱلصَّٰلِحِينَ ﴾
[آل عِمران: 114]

Iwo amakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku la chimaliziro, amalamulira zolungama ndi kuletsa zoipa ndipo amakhala ndi changu pochita ntchito zabwino,ndipo iwo ali pamodzi ndi anthu olungama

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يؤمنون بالله واليوم الآخر ويأمرون بالمعروف وينهون عن المنكر ويسارعون في الخيرات, باللغة نيانجا

﴿يؤمنون بالله واليوم الآخر ويأمرون بالمعروف وينهون عن المنكر ويسارعون في الخيرات﴾ [آل عِمران: 114]

Khaled Ibrahim Betala
“Amakhulupirira Allah ndi lsiku lomaliza; ndipo amalamulira (kuchita) zabwino ndikuletsa zoipa; ndipo amachita changu pa zinthu zabwino. Ndipo iwo ndi omwe ali mwa anthu abwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek