×

Fanizo la zimene amapereka mu umoyo wa m’dziko lino zili ngati mphepo 3:117 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:117) ayat 117 in Chichewa

3:117 Surah al-‘Imran ayat 117 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 117 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿مَثَلُ مَا يُنفِقُونَ فِي هَٰذِهِ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا كَمَثَلِ رِيحٖ فِيهَا صِرٌّ أَصَابَتۡ حَرۡثَ قَوۡمٖ ظَلَمُوٓاْ أَنفُسَهُمۡ فَأَهۡلَكَتۡهُۚ وَمَا ظَلَمَهُمُ ٱللَّهُ وَلَٰكِنۡ أَنفُسَهُمۡ يَظۡلِمُونَ ﴾
[آل عِمران: 117]

Fanizo la zimene amapereka mu umoyo wa m’dziko lino zili ngati mphepo ya chisanu imene imagwa m’minda ya anthu ochita zoipa ndi kuiononga. Mulungu sadawalakwire ayi koma iwo adadzilakwira okha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: مثل ما ينفقون في هذه الحياة الدنيا كمثل ريح فيها صر أصابت, باللغة نيانجا

﴿مثل ما ينفقون في هذه الحياة الدنيا كمثل ريح فيها صر أصابت﴾ [آل عِمران: 117]

Khaled Ibrahim Betala
“Fanizo la chimene akupereka mwaulere pa moyo uwu wa dziko lapansi, chili ngati mphepo yomwe mkati mwake muli chisanu chaukali, chagwera pa munda wa anthu omwe adadzichitira okha zoipa, n’kuuonongeratu. Si Allah amene adawachitira zoipa, koma iwo okha adadzichitira zoipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek