×

Zake za Mulungu ndi zinthu zonse zimene zili kumwamba ndi padziko lapansi. 3:129 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:129) ayat 129 in Chichewa

3:129 Surah al-‘Imran ayat 129 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 129 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَلِلَّهِ مَا فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَمَا فِي ٱلۡأَرۡضِۚ يَغۡفِرُ لِمَن يَشَآءُ وَيُعَذِّبُ مَن يَشَآءُۚ وَٱللَّهُ غَفُورٞ رَّحِيمٞ ﴾
[آل عِمران: 129]

Zake za Mulungu ndi zinthu zonse zimene zili kumwamba ndi padziko lapansi. Iye amakhululukira aliyense amene wamufuna ndi kulanga aliyense amene wamufuna. Mulungu ndi wokhululukira ndi wachisoni

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولله ما في السموات وما في الأرض يغفر لمن يشاء ويعذب من, باللغة نيانجا

﴿ولله ما في السموات وما في الأرض يغفر لمن يشاء ويعذب من﴾ [آل عِمران: 129]

Khaled Ibrahim Betala
“Zonse zakumwamba ndi zapansi nza Allah; amamkhululukira amene wamfuna, ndikumulanga amene wamfuna. Komatu Allah Ngokhululuka kwambiri, Ngwachisoni chosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek