×

Iwo amene adati: “Ndithudi Mulungu adavomera lonjezo lathu loti tisakhulupirire mwa Mtumwi 3:183 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:183) ayat 183 in Chichewa

3:183 Surah al-‘Imran ayat 183 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 183 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿ٱلَّذِينَ قَالُوٓاْ إِنَّ ٱللَّهَ عَهِدَ إِلَيۡنَآ أَلَّا نُؤۡمِنَ لِرَسُولٍ حَتَّىٰ يَأۡتِيَنَا بِقُرۡبَانٖ تَأۡكُلُهُ ٱلنَّارُۗ قُلۡ قَدۡ جَآءَكُمۡ رُسُلٞ مِّن قَبۡلِي بِٱلۡبَيِّنَٰتِ وَبِٱلَّذِي قُلۡتُمۡ فَلِمَ قَتَلۡتُمُوهُمۡ إِن كُنتُمۡ صَٰدِقِينَ ﴾
[آل عِمران: 183]

Iwo amene adati: “Ndithudi Mulungu adavomera lonjezo lathu loti tisakhulupirire mwa Mtumwi wina aliyense pokhapokha ngati iye atibweretsera nsembe yomwe idzawotchedwa ndi moto wochokera kumwamba.” Nena: “Ndithudi! Kudadza kwa inuAtumwi ena ine ndisanadze ndi zizindikiro zooneka ndi zina za zimene mwanenazi. Kodi ndi chifukwa chiyani mudawapha awa ngati zimene muli kunena ndi zoona?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين قالوا إن الله عهد إلينا ألا نؤمن لرسول حتى يأتينا بقربان, باللغة نيانجا

﴿الذين قالوا إن الله عهد إلينا ألا نؤمن لرسول حتى يأتينا بقربان﴾ [آل عِمران: 183]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene anenanso: “Allah Adatilamula ife kuti tisakhulupirire mtumiki aliyense mpaka atabwera ndi nsembe yopserezedwa ndi moto.” Nena: “Adakudzerani atumiki ndisanadze ndi zisonyezo zooneka ndi chimene mukunenachi. Nanga bwanji mudawapha, ngati mukunenadi zoona?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek