×

Ndi pamene angelo adati: “oh Maria! Ndithudi Mulungu ali kukupatsa nkhani yabwino 3:45 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:45) ayat 45 in Chichewa

3:45 Surah al-‘Imran ayat 45 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 45 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿إِذۡ قَالَتِ ٱلۡمَلَٰٓئِكَةُ يَٰمَرۡيَمُ إِنَّ ٱللَّهَ يُبَشِّرُكِ بِكَلِمَةٖ مِّنۡهُ ٱسۡمُهُ ٱلۡمَسِيحُ عِيسَى ٱبۡنُ مَرۡيَمَ وَجِيهٗا فِي ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةِ وَمِنَ ٱلۡمُقَرَّبِينَ ﴾
[آل عِمران: 45]

Ndi pamene angelo adati: “oh Maria! Ndithudi Mulungu ali kukupatsa nkhani yabwino ya Mawu ochokera kwa Iye amene dzina lake ndi Messiya, Yesu mwana wa Maria, wolemekezeka m’dziko lino ndi m’dziko limene lili nkudza ndipo adzakhala m’gulu la anthu okhala pafupi ndi Mulungu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ قالت الملائكة يامريم إن الله يبشرك بكلمة منه اسمه المسيح عيسى, باللغة نيانجا

﴿إذ قالت الملائكة يامريم إن الله يبشرك بكلمة منه اسمه المسيح عيسى﴾ [آل عِمران: 45]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukira) pamene angelo adati: “E iwe Mariya! Ndithu Allah akukuuza nkhani yabwino (kuti ubereka mwana popanda mwamuna koma kupyolera mu) liwu lochokera kwa Iye (Allah, lakuti: “Bereka,” ndipo nkubereka popanda kupezana ndi mwamuna). Dzina lake ndi Mesiya Isa (Yesu) mwana wa Mariya, adzakhala wolemekezeka pa dziko lapansi ndi pa tsiku lachimaliziro; ndiponso ndi mmodzi wa oyandikitsidwa kwa Allah
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek