×

oh Ambuye wathu! Musalole kuti mitima yathu isokere pamene Inu mwatilangiza ndipo 3:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:8) ayat 8 in Chichewa

3:8 Surah al-‘Imran ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 8 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿رَبَّنَا لَا تُزِغۡ قُلُوبَنَا بَعۡدَ إِذۡ هَدَيۡتَنَا وَهَبۡ لَنَا مِن لَّدُنكَ رَحۡمَةًۚ إِنَّكَ أَنتَ ٱلۡوَهَّابُ ﴾
[آل عِمران: 8]

oh Ambuye wathu! Musalole kuti mitima yathu isokere pamene Inu mwatilangiza ndipo tipatseni chisomo chanu. Ndithudi Inu ndinu opereka moolowa manja

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ربنا لا تزغ قلوبنا بعد إذ هديتنا وهب لنا من لدنك رحمة, باللغة نيانجا

﴿ربنا لا تزغ قلوبنا بعد إذ هديتنا وهب لنا من لدنك رحمة﴾ [آل عِمران: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“(Anzeruwo amanena): “ E Mbuye wathu! Musaikhotetse mitima yathu pambuyo potiongola. Tipatseni chifundo chochokera kwa Inu. Ndithudi, Inu Ndinu wopatsa kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek