×

Zinthu zoipa zalowa m’dziko ndiponso m’nyanja chifukwa cha ntchito za anthu zimene 30:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:41) ayat 41 in Chichewa

30:41 Surah Ar-Rum ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 41 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿ظَهَرَ ٱلۡفَسَادُ فِي ٱلۡبَرِّ وَٱلۡبَحۡرِ بِمَا كَسَبَتۡ أَيۡدِي ٱلنَّاسِ لِيُذِيقَهُم بَعۡضَ ٱلَّذِي عَمِلُواْ لَعَلَّهُمۡ يَرۡجِعُونَ ﴾
[الرُّوم: 41]

Zinthu zoipa zalowa m’dziko ndiponso m’nyanja chifukwa cha ntchito za anthu zimene amachita ndi manja awo. Mulungu akhoza kuwalawitsa chilango chifukwa cha ntchito zawo kuti mwina athe kutembenuka

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ظهر الفساد في البر والبحر بما كسبت أيدي الناس ليذيقهم بعض الذي, باللغة نيانجا

﴿ظهر الفساد في البر والبحر بما كسبت أيدي الناس ليذيقهم بعض الذي﴾ [الرُّوم: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Chisokonezo chaonekera pamtunda ndi panyanja chifukwa cha zimene manja a anthu achita, kuti awalawitse (chilango cha) zina zomwe adachita; kuti iwo atembenukire (kwa Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek