×

Ndithudi Ife tidatumiza, Atumwi kwa anthu awo iwe usanabadwe ndipo iwo adadza 30:47 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:47) ayat 47 in Chichewa

30:47 Surah Ar-Rum ayat 47 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 47 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿وَلَقَدۡ أَرۡسَلۡنَا مِن قَبۡلِكَ رُسُلًا إِلَىٰ قَوۡمِهِمۡ فَجَآءُوهُم بِٱلۡبَيِّنَٰتِ فَٱنتَقَمۡنَا مِنَ ٱلَّذِينَ أَجۡرَمُواْۖ وَكَانَ حَقًّا عَلَيۡنَا نَصۡرُ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ﴾
[الرُّوم: 47]

Ndithudi Ife tidatumiza, Atumwi kwa anthu awo iwe usanabadwe ndipo iwo adadza kwa iwo ndi chiphunzitso choyenera. Ife tidapereka chilango kwa anthu ochimwa ndipo kuthandiza anthu okhulupirira ndi udindo wosatha kwa Ife

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد أرسلنا من قبلك رسلا إلى قومهم فجاءوهم بالبينات فانتقمنا من الذين, باللغة نيانجا

﴿ولقد أرسلنا من قبلك رسلا إلى قومهم فجاءوهم بالبينات فانتقمنا من الذين﴾ [الرُّوم: 47]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo, ndithu tidatuma aneneri kwa anthu awo patsogolo pako. Choncho (mneneri aliyense) adawadzera anthu ake ndi maumboni oonekera poyera (osonyeza kuona kwawo, koma adawakana). Tero tidawawononga amene adalakwa. Ndikofunika kwa Ife kupulumutsa okhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek