×

Iwo amangodziwa zokhazo zimene amaziona za m’moyo uno koma za m’moyo umene 30:7 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:7) ayat 7 in Chichewa

30:7 Surah Ar-Rum ayat 7 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 7 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿يَعۡلَمُونَ ظَٰهِرٗا مِّنَ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا وَهُمۡ عَنِ ٱلۡأٓخِرَةِ هُمۡ غَٰفِلُونَ ﴾
[الرُّوم: 7]

Iwo amangodziwa zokhazo zimene amaziona za m’moyo uno koma za m’moyo umene uli nkudza, iwo safuna kumva china chilichonse cha izo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يعلمون ظاهرا من الحياة الدنيا وهم عن الآخرة هم غافلون, باللغة نيانجا

﴿يعلمون ظاهرا من الحياة الدنيا وهم عن الآخرة هم غافلون﴾ [الرُّوم: 7]

Khaled Ibrahim Betala
“Akudziwa zoonekera (zokhazokha) za moyo wa dziko lapansi (zomwe amadalira pa moyo wawo. Monga ulimi, malonda, zomangamanga ndi zina zotero). Ndipo iwo salabadira za tsiku la chimaliziro
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek