×

Iwe ukhoza kumusiya aliyense wa iwo amene wafuna ndipo ukhoza kutenga aliyense 33:51 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:51) ayat 51 in Chichewa

33:51 Surah Al-Ahzab ayat 51 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 51 - الأحزَاب - Page - Juz 22

﴿۞ تُرۡجِي مَن تَشَآءُ مِنۡهُنَّ وَتُـٔۡوِيٓ إِلَيۡكَ مَن تَشَآءُۖ وَمَنِ ٱبۡتَغَيۡتَ مِمَّنۡ عَزَلۡتَ فَلَا جُنَاحَ عَلَيۡكَۚ ذَٰلِكَ أَدۡنَىٰٓ أَن تَقَرَّ أَعۡيُنُهُنَّ وَلَا يَحۡزَنَّ وَيَرۡضَيۡنَ بِمَآ ءَاتَيۡتَهُنَّ كُلُّهُنَّۚ وَٱللَّهُ يَعۡلَمُ مَا فِي قُلُوبِكُمۡۚ وَكَانَ ٱللَّهُ عَلِيمًا حَلِيمٗا ﴾
[الأحزَاب: 51]

Iwe ukhoza kumusiya aliyense wa iwo amene wafuna ndipo ukhoza kutenga aliyense wa iwo amene wafuna ndi aliyense wa iwo amene udawasiya pa kanthawi kochepa. Palibe cholakwa kwa iwe pochita izi kuti maso awo azizire ndiponso onse asadandaule ndi zimene uwapatsa. Ndipo Mulungu amadziwa zinthu zonse zomwe zili m’mitima mwanu. Mulungu amadziwa zonse ndiponso ndi wopirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ترجي من تشاء منهن وتؤوي إليك من تشاء ومن ابتغيت ممن عزلت, باللغة نيانجا

﴿ترجي من تشاء منهن وتؤوي إليك من تشاء ومن ابتغيت ممن عزلت﴾ [الأحزَاب: 51]

Khaled Ibrahim Betala
“Ukhoza kumchedwetsa (posagona m’nyumba mwake) amene wam’funa pakati pa iwo ndi kumuyandikitsa kwa iwe amene wam’funa. Ndipo amene wam’funa mwa amene udawapatuka, palibe tchimo pa iwe. Kuchita izi kuchititsa kuti maso awo atonthole (mitima yawo ikondwe) ndipo asadandaule; ndi kuyanjana nacho chimene wawapatsa onse. Ndipo Allah akudziwa zimene zili m’mitima mwanu. Ndipo Allah Ngodziwa kwambiri, Ngoleza, (salanga mwachangu)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek