×

Ndipo musafoke pofunafuna mdani. Ngati inu mumva kuwawa nawonso, ndithudi, akumva kuwawa 4:104 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:104) ayat 104 in Chichewa

4:104 Surah An-Nisa’ ayat 104 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 104 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَلَا تَهِنُواْ فِي ٱبۡتِغَآءِ ٱلۡقَوۡمِۖ إِن تَكُونُواْ تَأۡلَمُونَ فَإِنَّهُمۡ يَأۡلَمُونَ كَمَا تَأۡلَمُونَۖ وَتَرۡجُونَ مِنَ ٱللَّهِ مَا لَا يَرۡجُونَۗ وَكَانَ ٱللَّهُ عَلِيمًا حَكِيمًا ﴾
[النِّسَاء: 104]

Ndipo musafoke pofunafuna mdani. Ngati inu mumva kuwawa nawonso, ndithudi, akumva kuwawa monga mmene mukuonera kuwawa inu. Koma inu muli ndi chiyembekezo chochokera kwa Mulungu chimene iwo alibe. Ndipo Mulungu ndi wodziwa ndi wanzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا تهنوا في ابتغاء القوم إن تكونوا تألمون فإنهم يألمون كما تألمون, باللغة نيانجا

﴿ولا تهنوا في ابتغاء القوم إن تكونوا تألمون فإنهم يألمون كما تألمون﴾ [النِّسَاء: 104]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo musachite ulesi kutsata anthu (omwe ndi adani), ngati mukumva kupweteka, iwonso akumva kupweteka monga momwe inu mukumvera kupweteka. Koma inu mukuyembekezera kwa Allah chomwe iwo sakuyembekezera. Ndipotu Allah Ngodziwa, Ngwanzeru
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek