×

IfesitidatumizeMtumwialiyense,komakutiatsatiridwe mwa lamulo la Mulungu. Ngati iwo adadzilakwitsa, akanadza kwa iwe kupempha 4:64 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:64) ayat 64 in Chichewa

4:64 Surah An-Nisa’ ayat 64 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 64 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَمَآ أَرۡسَلۡنَا مِن رَّسُولٍ إِلَّا لِيُطَاعَ بِإِذۡنِ ٱللَّهِۚ وَلَوۡ أَنَّهُمۡ إِذ ظَّلَمُوٓاْ أَنفُسَهُمۡ جَآءُوكَ فَٱسۡتَغۡفَرُواْ ٱللَّهَ وَٱسۡتَغۡفَرَ لَهُمُ ٱلرَّسُولُ لَوَجَدُواْ ٱللَّهَ تَوَّابٗا رَّحِيمٗا ﴾
[النِّسَاء: 64]

IfesitidatumizeMtumwialiyense,komakutiatsatiridwe mwa lamulo la Mulungu. Ngati iwo adadzilakwitsa, akanadza kwa iwe kupempha chikhululukiro cha Mulungu ndipo Mtumwi akadawapemphera chikhululukiro cha Mulungu. Iwo akadamupeza Iye wokhululuka ndi wa chisoni

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما أرسلنا من رسول إلا ليطاع بإذن الله ولو أنهم إذ ظلموا, باللغة نيانجا

﴿وما أرسلنا من رسول إلا ليطاع بإذن الله ولو أنهم إذ ظلموا﴾ [النِّسَاء: 64]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo sitidamtumize mtumiki aliyense koma kuti azimveredwa mwa lamulo la Allah. Ngati akadakudzera pamene adadzichitira okha zoipa, (chifukwa chokafuna chiweruzo cha satana) napempha chikhululuko kwa Allah (naye) Mtumiki nkuwapempheranso chikhululuko, ndithudi, akadampeza Allah ali Wolandira kulapa kwawo ali Wachisoni chosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek