×

Pali ponse pomwe mungakhale, imfa idzakupezani, ngakhale inu mutadzitsekera mkati mwa nsanja 4:78 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:78) ayat 78 in Chichewa

4:78 Surah An-Nisa’ ayat 78 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 78 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿أَيۡنَمَا تَكُونُواْ يُدۡرِككُّمُ ٱلۡمَوۡتُ وَلَوۡ كُنتُمۡ فِي بُرُوجٖ مُّشَيَّدَةٖۗ وَإِن تُصِبۡهُمۡ حَسَنَةٞ يَقُولُواْ هَٰذِهِۦ مِنۡ عِندِ ٱللَّهِۖ وَإِن تُصِبۡهُمۡ سَيِّئَةٞ يَقُولُواْ هَٰذِهِۦ مِنۡ عِندِكَۚ قُلۡ كُلّٞ مِّنۡ عِندِ ٱللَّهِۖ فَمَالِ هَٰٓؤُلَآءِ ٱلۡقَوۡمِ لَا يَكَادُونَ يَفۡقَهُونَ حَدِيثٗا ﴾
[النِّسَاء: 78]

Pali ponse pomwe mungakhale, imfa idzakupezani, ngakhale inu mutadzitsekera mkati mwa nsanja zolimba. Ndipo ngati zabwino ziwapeza, iwo amati: “Izi zachokera kwa Mulungu” koma ngati choipa chiwagwera, iwo amati: “Ichi ndi chochokera kwa iwe.” Nena: “Zinthu zonse zimachokera kwa Mulungu.” Kodi ndi chiani chawapeza anthu awa kuti sangathe kuzindikira china chiri chonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أينما تكونوا يدرككم الموت ولو كنتم في بروج مشيدة وإن تصبهم حسنة, باللغة نيانجا

﴿أينما تكونوا يدرككم الموت ولو كنتم في بروج مشيدة وإن تصبهم حسنة﴾ [النِّسَاء: 78]

Khaled Ibrahim Betala
“Paliponse pamene mungakhale imfa ikupezani ngakhale mutakhala m’malinga olimba, ndipo ngati ubwino utawafika (opembedza mafano ndi achiphamaso) amati: “Ubwinowu, ukuchokera kwa Allah.” Koma choipa chikawafikira, amati: “Ichi chachitika chifukwa cha iwe (Muhammad).” Nena: “Zonse zachokera kwa Allah.” Kodi ngotani anthu awa, sangathe kuzindikira nkhani
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek