×

Ndipo iwo sadzakhala ndi abwenzi oti awathandize kupatula Mulungu. Ndipo aliyense amene 42:46 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:46) ayat 46 in Chichewa

42:46 Surah Ash-Shura ayat 46 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 46 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿وَمَا كَانَ لَهُم مِّنۡ أَوۡلِيَآءَ يَنصُرُونَهُم مِّن دُونِ ٱللَّهِۗ وَمَن يُضۡلِلِ ٱللَّهُ فَمَا لَهُۥ مِن سَبِيلٍ ﴾
[الشُّوري: 46]

Ndipo iwo sadzakhala ndi abwenzi oti awathandize kupatula Mulungu. Ndipo aliyense amene Mulungu wamusocheza alibe wina womutsogolera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان لهم من أولياء ينصرونهم من دون الله ومن يضلل الله, باللغة نيانجا

﴿وما كان لهم من أولياء ينصرونهم من دون الله ومن يضلل الله﴾ [الشُّوري: 46]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo sadzakhala ndi athangati owapulumutsa (kuchilango cha Moto) kupatula Allah. Ndipo amene Allah wamusiya kuti asokere (chifukwa cha zochita zake zoipa) sangapeze njira (yopezera kulungama)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek