×

Kodi iwo sadayende padziko lapansi ndi kuona zimene zidawachitikira iwo amene adalipo 47:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:10) ayat 10 in Chichewa

47:10 Surah Muhammad ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 10 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿۞ أَفَلَمۡ يَسِيرُواْ فِي ٱلۡأَرۡضِ فَيَنظُرُواْ كَيۡفَ كَانَ عَٰقِبَةُ ٱلَّذِينَ مِن قَبۡلِهِمۡۖ دَمَّرَ ٱللَّهُ عَلَيۡهِمۡۖ وَلِلۡكَٰفِرِينَ أَمۡثَٰلُهَا ﴾
[مُحمد: 10]

Kodi iwo sadayende padziko lapansi ndi kuona zimene zidawachitikira iwo amene adalipo kale? Mulungu adaponya chionongeko pa iwo ndipo onse osakhulupirira adzaona mavuto a mtundu womwewo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفلم يسيروا في الأرض فينظروا كيف كان عاقبة الذين من قبلهم دمر, باللغة نيانجا

﴿أفلم يسيروا في الأرض فينظروا كيف كان عاقبة الذين من قبلهم دمر﴾ [مُحمد: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi sadayendeyende padziko nkuona kuti adali bwanji mapeto a amene adawatsogolera (monga Âdi ndi Samudi, ndi anthu a Luti ndi ena otero)? Allah adawaononga psiti, ndipo chilango ngati chimenecho chidzakhalanso kwa osakhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek