×

Ndithudi Mulungu adasangalala ndi anthu okhulupirira pamene iwo adakulonjeza patsinde pa mtengo 48:18 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Fath ⮕ (48:18) ayat 18 in Chichewa

48:18 Surah Al-Fath ayat 18 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Fath ayat 18 - الفَتح - Page - Juz 26

﴿۞ لَّقَدۡ رَضِيَ ٱللَّهُ عَنِ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ إِذۡ يُبَايِعُونَكَ تَحۡتَ ٱلشَّجَرَةِ فَعَلِمَ مَا فِي قُلُوبِهِمۡ فَأَنزَلَ ٱلسَّكِينَةَ عَلَيۡهِمۡ وَأَثَٰبَهُمۡ فَتۡحٗا قَرِيبٗا ﴾
[الفَتح: 18]

Ndithudi Mulungu adasangalala ndi anthu okhulupirira pamene iwo adakulonjeza patsinde pa mtengo kuti adzakhala ndi iwe ndipo Iye adadziwa zimene zidali m’mitima mwawo. Ndipo Iye adatumiza madalitso kwa iwo ndipo adawalipirira mwamsanga mphotho yopambana

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لقد رضي الله عن المؤمنين إذ يبايعونك تحت الشجرة فعلم ما في, باللغة نيانجا

﴿لقد رضي الله عن المؤمنين إذ يبايعونك تحت الشجرة فعلم ما في﴾ [الفَتح: 18]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu Allah adawayanja okhulupirira pamene amagwirana nawe (Mtumiki) chanza pansi pa mtengo pomwe amakulonjeza (kuti adzamenya nkhondo mpaka imfa) Allah adadziwa zomwe zidali m’mitima mwawo ndipo adatsitsa pa iwo kukhazikika (ndi kudekha;) ndipo adawalipira kupambana kwapafupi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek