×

Pamene iwo osakhulupirira adasunga chidani m’mitima mwawo, chidani cha nthawi ya chikunja, 48:26 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Fath ⮕ (48:26) ayat 26 in Chichewa

48:26 Surah Al-Fath ayat 26 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Fath ayat 26 - الفَتح - Page - Juz 26

﴿إِذۡ جَعَلَ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ فِي قُلُوبِهِمُ ٱلۡحَمِيَّةَ حَمِيَّةَ ٱلۡجَٰهِلِيَّةِ فَأَنزَلَ ٱللَّهُ سَكِينَتَهُۥ عَلَىٰ رَسُولِهِۦ وَعَلَى ٱلۡمُؤۡمِنِينَ وَأَلۡزَمَهُمۡ كَلِمَةَ ٱلتَّقۡوَىٰ وَكَانُوٓاْ أَحَقَّ بِهَا وَأَهۡلَهَاۚ وَكَانَ ٱللَّهُ بِكُلِّ شَيۡءٍ عَلِيمٗا ﴾
[الفَتح: 26]

Pamene iwo osakhulupirira adasunga chidani m’mitima mwawo, chidani cha nthawi ya chikunja, ndipo Mulungu adatumiza chisomo chake kwa Mtumwi wake ndi kwa anthu okhulupirira. Ndipo adawachititsa iwo kukhala omvera malamulo odziletsa ndipo adakhazikitsa bata kukhala pa iwo chifukwa adali oyenera kulilandira batalo. Ndipo Mulungu amadziwa chinthu china chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ جعل الذين كفروا في قلوبهم الحمية حمية الجاهلية فأنـزل الله سكينته, باللغة نيانجا

﴿إذ جعل الذين كفروا في قلوبهم الحمية حمية الجاهلية فأنـزل الله سكينته﴾ [الفَتح: 26]

Khaled Ibrahim Betala
“Pamene omwe sadakhulupirire adaika mkwiyo m’mitima, mkwiyo waumbuli, Allah adatsitsa chikhazikiko Chake ndi kudekha pa Mtumiki Wake ndi pa okhulupirira, ndipo adawalimbikitsa ndi mawu woopa Allah; ndipo adali eni mawuwo ndi oyenerana nawo. Ndipo Allah Ngodziwa chilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek