Quran with Chichewa translation - Surah Adh-Dhariyat ayat 26 - الذَّاريَات - Page - Juz 26
﴿فَرَاغَ إِلَىٰٓ أَهۡلِهِۦ فَجَآءَ بِعِجۡلٖ سَمِينٖ ﴾
[الذَّاريَات: 26]
﴿فراغ إلى أهله فجاء بعجل سمين﴾ [الذَّاريَات: 26]
Khaled Ibrahim Betala “Adatembenukira kwa akunyumba ake (mwakachetechete), ndipo adadza ndi nyama ya mwana wa ng’ombe yonona (yowotcha) |