×

Ndithudi onse amene amatsutsa Mulungu ndi Mtumwi wakeadzatsitsidwakwambirimongamomweadatsitsidwira iwo amene adalipo kale. 58:5 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mujadilah ⮕ (58:5) ayat 5 in Chichewa

58:5 Surah Al-Mujadilah ayat 5 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mujadilah ayat 5 - المُجَادلة - Page - Juz 28

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ يُحَآدُّونَ ٱللَّهَ وَرَسُولَهُۥ كُبِتُواْ كَمَا كُبِتَ ٱلَّذِينَ مِن قَبۡلِهِمۡۚ وَقَدۡ أَنزَلۡنَآ ءَايَٰتِۭ بَيِّنَٰتٖۚ وَلِلۡكَٰفِرِينَ عَذَابٞ مُّهِينٞ ﴾
[المُجَادلة: 5]

Ndithudi onse amene amatsutsa Mulungu ndi Mtumwi wakeadzatsitsidwakwambirimongamomweadatsitsidwira iwo amene adalipo kale. Ndipo Ife tatumiza zizindikiro zooneka. Ndipo anthu onse osakhulupirira adzalandira chilango chochititsa manyazi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين يحادون الله ورسوله كبتوا كما كبت الذين من قبلهم وقد, باللغة نيانجا

﴿إن الذين يحادون الله ورسوله كبتوا كما كبت الذين من قبلهم وقد﴾ [المُجَادلة: 5]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene akutsutsana ndi Allah kudzanso Mthenga Wake, ayalutsidwa monga momwe adayalutsidwira amene adalipo patsogolo pawo; ndithu tavumbulutsa Ayah zolongosola, momveka (pa zololedwa ndi zoletsedwa). Ndipo chilango choyalutsa chili pa osakhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek