×

Nena: “Ine sindili kukuuzani kuti ndili ndi chuma cha Mulungu kapena kuti 6:50 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-An‘am ⮕ (6:50) ayat 50 in Chichewa

6:50 Surah Al-An‘am ayat 50 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-An‘am ayat 50 - الأنعَام - Page - Juz 7

﴿قُل لَّآ أَقُولُ لَكُمۡ عِندِي خَزَآئِنُ ٱللَّهِ وَلَآ أَعۡلَمُ ٱلۡغَيۡبَ وَلَآ أَقُولُ لَكُمۡ إِنِّي مَلَكٌۖ إِنۡ أَتَّبِعُ إِلَّا مَا يُوحَىٰٓ إِلَيَّۚ قُلۡ هَلۡ يَسۡتَوِي ٱلۡأَعۡمَىٰ وَٱلۡبَصِيرُۚ أَفَلَا تَتَفَكَّرُونَ ﴾
[الأنعَام: 50]

Nena: “Ine sindili kukuuzani kuti ndili ndi chuma cha Mulungu kapena kuti ndimadziwa zinthu zobisika kapena kuti ine ndine mngelo. Ine sinditsatira china chilichonse kupatula zokhazo zimene zavumbulutsidwa kwa ine.” Nena: “Kodi munthu wakhungu ndi munthu openya angafanane? Kodi inu simungaganize?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل لا أقول لكم عندي خزائن الله ولا أعلم الغيب ولا أقول, باللغة نيانجا

﴿قل لا أقول لكم عندي خزائن الله ولا أعلم الغيب ولا أقول﴾ [الأنعَام: 50]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek