×

Ndithudi Mulungu amakonda iwo amene amamenya nkhondo ndi cholinga chokhazikitsa ulamuliro wake 61:4 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah As-saff ⮕ (61:4) ayat 4 in Chichewa

61:4 Surah As-saff ayat 4 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah As-saff ayat 4 - الصَّف - Page - Juz 28

﴿إِنَّ ٱللَّهَ يُحِبُّ ٱلَّذِينَ يُقَٰتِلُونَ فِي سَبِيلِهِۦ صَفّٗا كَأَنَّهُم بُنۡيَٰنٞ مَّرۡصُوصٞ ﴾
[الصَّف: 4]

Ndithudi Mulungu amakonda iwo amene amamenya nkhondo ndi cholinga chokhazikitsa ulamuliro wake molimba, m’magulu, ngati chipupa cha miyala

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الله يحب الذين يقاتلون في سبيله صفا كأنهم بنيان مرصوص, باللغة نيانجا

﴿إن الله يحب الذين يقاتلون في سبيله صفا كأنهم بنيان مرصوص﴾ [الصَّف: 4]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu Allah amakonda amene akumenya nkhondo pa njira Yake (yofalitsa chipembedzo Chake), ali pa mzere (umodzi) uku ali monga chomanga, chomangika mwamphamvu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek