×

Ndiye amene watumiza Mtumwi wake ndi ulangizi ndiponso chipembedzo choonadi kuti chikhale 61:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah As-saff ⮕ (61:9) ayat 9 in Chichewa

61:9 Surah As-saff ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah As-saff ayat 9 - الصَّف - Page - Juz 28

﴿هُوَ ٱلَّذِيٓ أَرۡسَلَ رَسُولَهُۥ بِٱلۡهُدَىٰ وَدِينِ ٱلۡحَقِّ لِيُظۡهِرَهُۥ عَلَى ٱلدِّينِ كُلِّهِۦ وَلَوۡ كَرِهَ ٱلۡمُشۡرِكُونَ ﴾
[الصَّف: 9]

Ndiye amene watumiza Mtumwi wake ndi ulangizi ndiponso chipembedzo choonadi kuti chikhale chapamwamba pa zipembedzo zina zonse ngakhale kuti anthu osakhulupirira sakondwera nazo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: هو الذي أرسل رسوله بالهدى ودين الحق ليظهره على الدين كله ولو, باللغة نيانجا

﴿هو الذي أرسل رسوله بالهدى ودين الحق ليظهره على الدين كله ولو﴾ [الصَّف: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“Iye ndi amene adatuma Mtumiki Wake (Muhammad{s.a.w}) ndi chiongoko ndi chipembedzo choona, kuti achiike pamwamba pa zipembedzo zonse, ngakhale kuti ophatikiza Allah ndi mafano zikuwaipira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek