×

Ichi ndi chifukwa chakuti kunadza kwa iwo Atumwi amene adali ndi zizindikiro 64:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taghabun ⮕ (64:6) ayat 6 in Chichewa

64:6 Surah At-Taghabun ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taghabun ayat 6 - التغَابُن - Page - Juz 28

﴿ذَٰلِكَ بِأَنَّهُۥ كَانَت تَّأۡتِيهِمۡ رُسُلُهُم بِٱلۡبَيِّنَٰتِ فَقَالُوٓاْ أَبَشَرٞ يَهۡدُونَنَا فَكَفَرُواْ وَتَوَلَّواْۖ وَّٱسۡتَغۡنَى ٱللَّهُۚ وَٱللَّهُ غَنِيٌّ حَمِيدٞ ﴾
[التغَابُن: 6]

Ichi ndi chifukwa chakuti kunadza kwa iwo Atumwi amene adali ndi zizindikiro zooneka koma iwo adati: “Kodi ife tizitsogozedwa ndi anthu anzathu?” Kotero iwo sanakhulupilire ndipo anabwerera m’mbuyo. Koma Mulungu sasowa kanthu. Ndithudi Mulungu ndi Mwini wa chilichonse ndi Mwini ulemerero wonse. Al Taghabun

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ذلك بأنه كانت تأتيهم رسلهم بالبينات فقالوا أبشر يهدوننا فكفروا وتولوا واستغنى, باللغة نيانجا

﴿ذلك بأنه كانت تأتيهم رسلهم بالبينات فقالوا أبشر يهدوننا فكفروا وتولوا واستغنى﴾ [التغَابُن: 6]

Khaled Ibrahim Betala
“Zimenezo nchifukwa chakuti atumiki awo amawadzera ndi zozizwitsa koma iwo amanena (mwachipongwe): “Ha! Anthu anzathu (onga ife) angationgole?” Choncho sadakhulupirire (utumiki wawo) ndipo adanyoza (choonadi) potero Allah adawasiya (ndi kupanda chikhulupiliro kwawo) ndipo Allah Ngokwanira ndiponso Ngoyamikidwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek