×

Mose adati: “Ambuye wanga! Ndikhululukireni ine pamodzi ndi m’bale wanga ndipo tilowetseni 7:151 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:151) ayat 151 in Chichewa

7:151 Surah Al-A‘raf ayat 151 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 151 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿قَالَ رَبِّ ٱغۡفِرۡ لِي وَلِأَخِي وَأَدۡخِلۡنَا فِي رَحۡمَتِكَۖ وَأَنتَ أَرۡحَمُ ٱلرَّٰحِمِينَ ﴾
[الأعرَاف: 151]

Mose adati: “Ambuye wanga! Ndikhululukireni ine pamodzi ndi m’bale wanga ndipo tilowetseni m’chisoni chanu chifukwa Inu ndinu oonetsa chisoni kwambiri kuposa onse omwe amaonetsa chisoni.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال رب اغفر لي ولأخي وأدخلنا في رحمتك وأنت أرحم الراحمين, باللغة نيانجا

﴿قال رب اغفر لي ولأخي وأدخلنا في رحمتك وأنت أرحم الراحمين﴾ [الأعرَاف: 151]

Khaled Ibrahim Betala
“(Mûsa) adati: “Mbuye wanga! Ndikhululukireni ine ndi m’bale wanga ndipo tilowetseni m’chifundo Chanu. Inu Ndinu Achifundo kuposa achifundo onse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek