×

Ndi pamene Ambuye wako adalamula kuti adzawatumizira, mpaka tsiku la chiweruzo, iwo 7:167 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:167) ayat 167 in Chichewa

7:167 Surah Al-A‘raf ayat 167 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 167 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿وَإِذۡ تَأَذَّنَ رَبُّكَ لَيَبۡعَثَنَّ عَلَيۡهِمۡ إِلَىٰ يَوۡمِ ٱلۡقِيَٰمَةِ مَن يَسُومُهُمۡ سُوٓءَ ٱلۡعَذَابِۗ إِنَّ رَبَّكَ لَسَرِيعُ ٱلۡعِقَابِ وَإِنَّهُۥ لَغَفُورٞ رَّحِيمٞ ﴾
[الأعرَاف: 167]

Ndi pamene Ambuye wako adalamula kuti adzawatumizira, mpaka tsiku la chiweruzo, iwo amene azibweretsa mazunzo ndi mnyozo pa iwo. Ndithudi Ambuye wako ndi wachangu polanga. Ndipo, ndithudi, Iye ndi wokhululukira ndipo ndi wachisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ تأذن ربك ليبعثن عليهم إلى يوم القيامة من يسومهم سوء العذاب, باللغة نيانجا

﴿وإذ تأذن ربك ليبعثن عليهم إلى يوم القيامة من يسومهم سوء العذاب﴾ [الأعرَاف: 167]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (akumbutse) pamene Mbuye wako analengeza (kuti) ndithu adzawatumizira iwo (Ayuda) anthu mpaka tsiku la Qiyâma, omwe adzawazunza ndi mazunzo oipa. Ndithu Mbuye wako ngofulumira kulanga, ndipo ndithu palibe chikaiko, Iye Ngokhululuka kwambiri, Ngwachifundo chambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek