×

Ndithudi, Ife tanalenga majini ndi anthu ambiri kuti akalowe ku Gahena. Iwo 7:179 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:179) ayat 179 in Chichewa

7:179 Surah Al-A‘raf ayat 179 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 179 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿وَلَقَدۡ ذَرَأۡنَا لِجَهَنَّمَ كَثِيرٗا مِّنَ ٱلۡجِنِّ وَٱلۡإِنسِۖ لَهُمۡ قُلُوبٞ لَّا يَفۡقَهُونَ بِهَا وَلَهُمۡ أَعۡيُنٞ لَّا يُبۡصِرُونَ بِهَا وَلَهُمۡ ءَاذَانٞ لَّا يَسۡمَعُونَ بِهَآۚ أُوْلَٰٓئِكَ كَٱلۡأَنۡعَٰمِ بَلۡ هُمۡ أَضَلُّۚ أُوْلَٰٓئِكَ هُمُ ٱلۡغَٰفِلُونَ ﴾
[الأعرَاف: 179]

Ndithudi, Ife tanalenga majini ndi anthu ambiri kuti akalowe ku Gahena. Iwo ali ndi mitima imene sangathe kuzindikira, ali ndi maso amene sangathe kuona, ali ndi makutu amene sangathe kumva ayi. Iwo ali ngati ng’ombe. Iyai! Iwo ndi osochera kwambiri. Amenewa! Ndi nkhutukumve

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد ذرأنا لجهنم كثيرا من الجن والإنس لهم قلوب لا يفقهون بها, باللغة نيانجا

﴿ولقد ذرأنا لجهنم كثيرا من الجن والإنس لهم قلوب لا يفقهون بها﴾ [الأعرَاف: 179]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi, ziwanda zambiri ndi anthu tidawalengera kukalowa ku (Moto wa) Jahannam. Mitima ali nayo koma sazindikira nayo kanthu; ndipo maso ali nawo koma sapenyera nawo (zodabwitsa za Allah); ndipo makutu ali nawo koma samvera nawo (zowapindulitsa). Iwo ali ngati ziweto, kapena iwo ndi osokera zedi kuposa Ziweto. Iwo ndi osalabadira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek