×

Ndipo pamene Mutu uvumbulutsidwa kuwauza kuti akhulupirire mwa Mulungu ndi kuti amenye 9:86 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:86) ayat 86 in Chichewa

9:86 Surah At-Taubah ayat 86 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 86 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿وَإِذَآ أُنزِلَتۡ سُورَةٌ أَنۡ ءَامِنُواْ بِٱللَّهِ وَجَٰهِدُواْ مَعَ رَسُولِهِ ٱسۡتَـٔۡذَنَكَ أُوْلُواْ ٱلطَّوۡلِ مِنۡهُمۡ وَقَالُواْ ذَرۡنَا نَكُن مَّعَ ٱلۡقَٰعِدِينَ ﴾
[التوبَة: 86]

Ndipo pamene Mutu uvumbulutsidwa kuwauza kuti akhulupirire mwa Mulungu ndi kuti amenye nkhondo limodzi ndi Mtumwi, anthu olemera pakati pawo amakupempha kuti, asakamenye nawo ndipo amati: “Tisiye ife tikhale pamodzi ndi anthu okhala m’mbuyo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذا أنـزلت سورة أن آمنوا بالله وجاهدوا مع رسوله استأذنك أولو الطول, باللغة نيانجا

﴿وإذا أنـزلت سورة أن آمنوا بالله وجاهدوا مع رسوله استأذنك أولو الطول﴾ [التوبَة: 86]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Sura ikavumbulutsidwa (yonena kuti): “Mkhulupirireni Allah ndi kumenya nkhondo (chifukwa cha chipembedzo Chake) pamodzi ndi Mtumiki Wake,” opeza bwino mwa iwo akukupempha chilolezo (kuti asapite ku nkhondo), ndipo akuti: “Tisiye tikhale pamodzi ndi okhala (otsalira m’mbuyo).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek